Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

  1. Home   »  
  2. Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

 

LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
Lemekeza Mulungu Mwana,
Lemekeza Mulungu Mzimu,
Mulungu Mmodzi ndi wamkulu,
Lemekeza, lemekeza
Mulungu wathu yemweyo.

Mlemekeze, anakonda
Natitsuka m’mtima mwathu;
Anatiwombola ife
Tikakhale ndi chifumu.
Lemekeza, lemekeza
Yesu Mbuye Nsembeyo.

Lemekeza Mfumu yathu,
Mfumu ya mipingo yonse,
Ipambana anthu onse
Akumwamba ndi apansi.
Lemekeza, lemekeza
Mfumu ya mafumuyo

Post navigation

Previous: Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
Next: Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version