Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

 

NDI Aleluya imbirani,
“Tate wathu wa Kumwamba,
Analenga zonse;
Chifundo chake chachikulu,
Nzeru, mphamvu ndi ufumu,
Tiyamike tonse.

Ndi Aleluya imbirani,
Yesu Khrisitu Mpulumutsi,
Anachoka kwawo;
Nakhala munthu pansi pano,
Nasawuka, natifera,
Natisiira mawu.

Ndi Aleluya imbirani,
Mzimu wake wakuyera,
Amakhala nafe:
Atilangiza za Mulungu,
Nayeretsanso mitima,
Ya Akhrisitu ife.

Mulungu wathu tiyamika,
“Tate, Mwana,
Mzimu yemwe,
Aleluya Inu;
Woyera Inu, ndi wamphamvu,
Muyenera anthu onse,
Agwadire Inu.

Post navigation

Previous: Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
Next: Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hello world!
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version