Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

 

NDI Aleluya imbirani,
“Tate wathu wa Kumwamba,
Analenga zonse;
Chifundo chake chachikulu,
Nzeru, mphamvu ndi ufumu,
Tiyamike tonse.

Ndi Aleluya imbirani,
Yesu Khrisitu Mpulumutsi,
Anachoka kwawo;
Nakhala munthu pansi pano,
Nasawuka, natifera,
Natisiira mawu.

Ndi Aleluya imbirani,
Mzimu wake wakuyera,
Amakhala nafe:
Atilangiza za Mulungu,
Nayeretsanso mitima,
Ya Akhrisitu ife.

Mulungu wathu tiyamika,
“Tate, Mwana,
Mzimu yemwe,
Aleluya Inu;
Woyera Inu, ndi wamphamvu,
Muyenera anthu onse,
Agwadire Inu.

Post navigation

Previous: Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
Next: Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version