Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,

Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,

 

IMFA ya Mwana wa Mulungu,
Inali yomvetsatu chisoni;
Anatifera pa mtandapo,
Kutiwombola kumachimo.

Chinsalu cha m’kachisi
Chinang’ambika pakati
Ndi pempho la
M’dzina la! Tate,
Ndi Mwana ndi Mzimunso.

Mbuye Yesu ponka
Kumwamba,
Nanena, “ndikupita kwa “Tate;
Kukakukonzerani malo,
Ndipo Ine ndidzabweranso.

“Koma mudzalandira mphamvu,
Mzimu Woyera ‘tadza pa Inu”;
Ndipo tonsefe ndife mboni,
Kutitu Mzimu ndi Nkhosweyo.

Post navigation

Previous: Hymn 47 YESU panjirayo,
Next: Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version