Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

  1. Home   »  
  2. Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

 

ONA Mwanawankhosayo
Wakuseza zakuipa zathu zonse.

Mwana wankhosa
Watisenzera
Zakuipa zathu zonse.

Anazenza m’thupi mwake;
Pakukhomedwa pa mtanda anali duu.

Ona pamtanda Yesuyo
Anabvutika chifukwa cha anthu’fe.

Imva kulira kwa Yesu
Pamene anasiyidwa muimfayo.

M’mwazi wake tisambamo;
Zichotsedwa zakuipa zathu zonse.

(Ona Mwana wa nkhosayo
Wakusenza zakuipa, zathu zonse.)

Post navigation

Previous: Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
Next: Hymn 50 PAUSIKU uja,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 1490 Musachitenso nthantha ‘yi,
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version