Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

  1. Home   »  
  2. Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

 

ONA Mwanawankhosayo
Wakuseza zakuipa zathu zonse.

Mwana wankhosa
Watisenzera
Zakuipa zathu zonse.

Anazenza m’thupi mwake;
Pakukhomedwa pa mtanda anali duu.

Ona pamtanda Yesuyo
Anabvutika chifukwa cha anthu’fe.

Imva kulira kwa Yesu
Pamene anasiyidwa muimfayo.

M’mwazi wake tisambamo;
Zichotsedwa zakuipa zathu zonse.

(Ona Mwana wa nkhosayo
Wakusenza zakuipa, zathu zonse.)

Post navigation

Previous: Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
Next: Hymn 50 PAUSIKU uja,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version