Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

  1. Home   »  
  2. Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,

 

NDI MISOZI, ndi chisoni,
Ndiliratu kwa Inu Yesu;
Ndi chifundo chandigwira,
Ndilira kutí ndili wanu

E! Kwa Inu, E! Kwa Inu!
Ndilira kuti ndili wanu.

Mbuye Yesu ndi Atate,
Mundiwona ndili wosowa;
Ndimasowa Mzimu wanu,
Kuinga zonse za mumtima.

Mtenderewo, wosanyenga,
Ndilira ine m’mtima mwanga;
Kundimvetsa chimwemwetu,
Ndilira ine m’mtima mwanga.

Kalekale ndinathawa,
Ndinakana kumvera Inu;
Koma lero ndamva kuti,
Muli mwini wake wa moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
Next: Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hello world!
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version