Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

  1. Home   »  
  2. Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

 

MULI ndi ludzu, idzani
Kumadzi amoyo
Imwani monse kolere
Kuchitsime konko.

Munka kangati kulaŵa
Madzi onyengera?
Musataye mphamvu yanu,
Musataye chuma.

Imvani, Yesu akuti;
“Chuma ndili nacho,
Landirani, yemwe amva
Akhale ndi moyo.”

Funani Mlungu tsopano.
Akulindirani;
Iye ndiye wachifundo,
Akulandirani.

Ali wokhululukira;
Imvani ananu:
Mtima wake usiyana
Ndi mitima yathu.

Monga m’Mwamba mupambana
Zonse pansi pano;
Choncho maganizo ake
Apitira athu.

Anthu onse a padziko
Adzamvera Mlungu:
Adzakhala ndi chimwemwe,
Nadzamtama ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
Next: Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version