Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

  1. Home   »  
  2. Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani

 

MULI ndi ludzu, idzani
Kumadzi amoyo
Imwani monse kolere
Kuchitsime konko.

Munka kangati kulaŵa
Madzi onyengera?
Musataye mphamvu yanu,
Musataye chuma.

Imvani, Yesu akuti;
“Chuma ndili nacho,
Landirani, yemwe amva
Akhale ndi moyo.”

Funani Mlungu tsopano.
Akulindirani;
Iye ndiye wachifundo,
Akulandirani.

Ali wokhululukira;
Imvani ananu:
Mtima wake usiyana
Ndi mitima yathu.

Monga m’Mwamba mupambana
Zonse pansi pano;
Choncho maganizo ake
Apitira athu.

Anthu onse a padziko
Adzamvera Mlungu:
Adzakhala ndi chimwemwe,
Nadzamtama ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
Next: Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version