Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

 

MBUYANGA Yesu,
mundigwire dzanja.
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Sindikaopa kanthu kena ’yi.

Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.

Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Lakuwalitsa m’mtima momwemu.

Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Pamene ine ndimwalirapo.
Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
Next: Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version