Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

  1. Home   »  
  2. Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

 

MBUYANGA Yesu, mundigwire
Dzanja.
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Sindikaopa kanthu kena ’yi.

Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.

Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Lakuwalitsa m’mtima momwemu.

Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Pamene ine ndimwalirapo.
Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
Next: Hymn 250 MBUYANGA Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version