Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu

 

MUMZINDA wa Mulungu
Moyera mulimo,
Ndiye amathu omwe
Olera ifewo;
Mitima yathu yomwe
Ikondwereratu,
Nikhala nawo Mzinda
Wakukongolawu.

Akondwerera anthu Zokoma zonsezi
Za midzi ya padziko
Lapansi lonseli;
Mtendere wake koma
Wa Mzinda wathuwo
Upambanditsa zonse
Zapansi pomwepo.

Ndi nkhondo ikaleka
Kwa Mlungu komweko,
Ndi ukapolo watha,
Udani wathanso;
Ndi zakuopsa zonse
Ndi zosauka zii!
Ndi mwayi wa kwa Mlungu
Udzoza mutu tho!

Post navigation

Previous: Hymn 328 KULIBE vuto
Next: Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version