Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

  1. Home   »  
  2. Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

 

MONGA zomera zonsezo
Zikula ponsepo,
Mulungu mumeretsazo,
Momwemo anawo.

Munali mwana, Yesu ’Nu
Wamng’ono kalelo,
Ndi munakula m’msinkhu ndi
Kutama ’Tatewo.

Ndi ife tinga, mbewuzo
Zomera m’mundawo;
Mumtima mutidyetsedi,
Tikule bwinomo;

Ndi kutsukidwa m’mwazimo
Mumtima mwathu mbee,
Tionetsedwe konseko
A Mlungu ana ’ke.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version