Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,

 

PANTHAWI yakufa Ambuye,
Anthu ananena:
“Dzipulumutsetu pamtandapo.”

(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O) Anafuula;
(M) Yesu ndi mawu aakulu,
(O)Anafuula;
“Eloyi, Eloyi
Mulungu wanga,
Mwandisiiranji,
Mwandisiiranji?”

Imfa ya Bwenzi lathu Yesu,
Yomvetsa chisoni;
Ophunzira onse anathaŵa.

Pamene anakhomedwatu,
Pamtanda Yesuyo;
Zoipa zathu zinam’psinja ‘Ye.

Imfa yake ndi yopambana,
Yotipulumutsa;
Yotitengera ife mtendere.

Post navigation

Previous: Hymn 50 PAUSIKU uja,
Next: Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version