Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

  1. Home   »  
  2. Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 256 NGATI mtima sumakonda

 

NGATI mtima sumakonda
Yesu supumula bwino;
Mbuye, suwu mtima wanga,
Ndiwo wanu, mulandire.

Dziko lonse ndilitaya;
Ndikondetsa Yesu Mbuye;
An’komera kopambana
Andikondweretsa ndiye.

Ndakudani, mnandikonda
Ndi kukhetsa mwazi wanu.
Simuleka kundikonda;
Ine sindidzalekanso.

Mndisungire mtima wanga,
Uzikhulupira Inu,
Kuti moyo wanga wonse
Ubisaletu mwa Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
Next: Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version