Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

 

NDALIMVA dziko la m’talimo,
Munthu sangathe kulisimba;
Malowo awala koposa,
Ndi Yesu tidzakhala naye.

Komweko, komweko,
Ndi Yesu tidzakhala naye.

Musazengereze anthuni,
Chimwemwe uko chilipodi;
Anthuni, mudzalandiradi,
Ndi Yesu mudzakhala naye.

Mwana’we pereka mtima’ko,
Akuchotsere zoipazo;
Udzakhala wokondweradi,
E! n’kwabwino lola mwana ‘we.

Idzani, mverani, lapani,
Chipulumutso chilipodi;
Kwa Yesu yemwe wofera ‘nu,
Ndi Yesu mudzanka
Kumwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
Next: Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version