Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

  1. Home   »  
  2. Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

 

PEMPHERO ndiko kufuna,
Kulakalakatu;
Ndi monga moto liyaka
Mumtima wa munthu.

Pemphero ndiko kulira,
Ngakhale misozi,
Kupenyetsetsa Kumwamba,
Mulungu mpafupi.

Pemphero ndiko kufuna
Kwa mwana wamng’ono;
Ndiponso mawu amphamvu
A munthu wamvanu.

Pemphero ndiwo mweyawo
Apuma akristu;
Ndi mapemphero tiloŵa
Dziko la imfalo.

Mutiphunzitse, Mbuyathu,
Kupempha kotero,
Kuyandikira kwa Mlungu
Ndi mtima wabwino.

Post navigation

Previous: Hymn 345 ATATE, ndipempha
Next: Hymn 347 YESU, ndipemphera

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version