Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

  1. Home   »  
  2. Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

 

PEMPHERO ndiko kufuna,
Kulakalakatu;
Ndi monga moto liyaka
Mumtima wa munthu.

Pemphero ndiko kulira,
Ngakhale misozi,
Kupenyetsetsa Kumwamba,
Mulungu mpafupi.

Pemphero ndiko kufuna
Kwa mwana wamng’ono;
Ndiponso mawu amphamvu
A munthu wamvanu.

Pemphero ndiwo mweyawo
Apuma akristu;
Ndi mapemphero tiloŵa
Dziko la imfalo.

Mutiphunzitse, Mbuyathu,
Kupempha kotero,
Kuyandikira kwa Mlungu
Ndi mtima wabwino.

Post navigation

Previous: Hymn 345 ATATE, ndipempha
Next: Hymn 347 YESU, ndipemphera

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version