Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 345 ATATE, ndipempha

  1. Home   »  
  2. Hymn 345 ATATE, ndipempha

Hymn 345 ATATE, ndipempha

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 345 ATATE, ndipempha

 

ATATE, ndipempha
Tsopano mundimvere,
Ndipempha kuti mundithandize.

Ine ndili munthu
Wochimwa pansi pano,
Munditsuke Mbuye, ndiyeretu.

Ndalema ndathodwa
Ndi zinthu zapadziko,
Zakhalatu goli londimanga.

Yesu Mfumu Inu
Mumandiuza kuti:
“Pemphera, ndipo udzalandira.”

Ndipempha, Ambuye,
Mundidzaze n’chikondi,
Mtima wangawu ukukondeni.

Post navigation

Previous: Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
Next: Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version