Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

 

UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
Inde, moyo tsopanopanotu;
Wolakwira upenye kwa Yesu Mbuyeyo,
Kuwombola naferatu ‘we.

Ona! Ona! Onatu!
Kuli moyo kwa yense
Apenya Yesuyo,
Wakuferatu pamtandapo.

Anasenzapo bwanji uchimo wonsewo,
Ngati wanu pa Yesu sulipo?
Bwanji mwazi wakhetsa kutsuka ifetu,
Ngati uwu sutikwanako?

Zilepheradi zonse kugula moyowo,
Koma mwazi wa Yesu Mbuyeyo;
Khulupi’ra mwamphamvu ya
Mlungu wathuyi,
Kuyeretsa’we m’mtima’komo.

Anatheradi pa mtanda ntchito zonsezi,
Zowombola mizimu yathuyi;
Ndipo yense akadza
Mokondwakondwadi,
Moyo apeza kwa Yesuko.

Post navigation

Previous: Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
Next: Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version