Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

 

AMBUYE, m’imfamo
Munandikonda ine;
Sindikaniza ’Nu
Kanthu konse ’yi.
Ndimagwadira ’nu.
Ndikonda m’mtimamu,
Ndidzaperekatu
Nsembe yangayi.

Kumwamba kwanuko
Mundipempherere;
Ndikhulupirako,
N’dzalandiradi;
Ndisenze mtandawo,
Ndikhale mboniyo,
Ndiperekeko
Mitoloyi.

Ndikhumba mtimawo
Wofatsa ndithu,
Kuti ndiyambe ’ne
Ntchito zanuzi;
Akusokerawo,
Abwere kwawoko,
Inde,kwanutu.

Zambiri zangazo
Mnandipatsa kale,
Ndibweza zonsezi
Kwa Mbuyanga ’Nu;
Ndikadzaona ’Nu,
Mbuye wabwinotu,
Nsembe yokomatu
Ndidzakhalabe

Post navigation

Previous: Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
Next: Hymn 232 WAFUNAFUNA ine

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version