Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

 

AMBUYE, m’imfamo
Munandikonda ine;
Sindikaniza ’Nu
Kanthu konse ’yi.
Ndimagwadira ’nu.
Ndikonda m’mtimamu,
Ndidzaperekatu
Nsembe yangayi.

Kumwamba kwanuko
Mundipempherere;
Ndikhulupirako,
N’dzalandiradi;
Ndisenze mtandawo,
Ndikhale mboniyo,
Ndiperekeko
Mitoloyi.

Ndikhumba mtimawo
Wofatsa ndithu,
Kuti ndiyambe ’ne
Ntchito zanuzi;
Akusokerawo,
Abwere kwawoko,
Inde,kwanutu.

Zambiri zangazo
Mnandipatsa kale,
Ndibweza zonsezi
Kwa Mbuyanga ’Nu;
Ndikadzaona ’Nu,
Mbuye wabwinotu,
Nsembe yokomatu
Ndidzakhalabe

Post navigation

Previous: Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
Next: Hymn 232 WAFUNAFUNA ine

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version