Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

  1. Home   »  
  2. Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo

 

AMBUYE, m’imfamo
Munandikonda ine;
Sindikaniza ’Nu
Kanthu konse ’yi.
Ndimagwadira ’nu.
Ndikonda m’mtimamu,
Ndidzaperekatu
Nsembe yangayi.

Kumwamba kwanuko
Mundipempherere;
Ndikhulupirako,
N’dzalandiradi;
Ndisenze mtandawo,
Ndikhale mboniyo,
Ndiperekeko
Mitoloyi.

Ndikhumba mtimawo
Wofatsa ndithu,
Kuti ndiyambe ’ne
Ntchito zanuzi;
Akusokerawo,
Abwere kwawoko,
Inde,kwanutu.

Zambiri zangazo
Mnandipatsa kale,
Ndibweza zonsezi
Kwa Mbuyanga ’Nu;
Ndikadzaona ’Nu,
Mbuye wabwinotu,
Nsembe yokomatu
Ndidzakhalabe

Post navigation

Previous: Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
Next: Hymn 232 WAFUNAFUNA ine

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version