Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

  1. Home   »  
  2. Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

 

KWACHA lero kwati mbee,
Tsiku la Mulunguli;
Dzuŵa liŵaliradi
Thambo ndi zapansipa
Upumira mpweyawu
Wa Mulungu konseku.

M’nyumba yanu, Mlungu, ’yi
Tisonkhana teretu,
Ndi mitundu yonseyi
Tikulambireni ’Nu:
Yesu Mbuye wathuyo
Ndiye Mfumu ponsepo.

Inu Mlungu kalelo
Mutalenga zonsezi
Munapuma tsikulo;
Tipumadi ifenso.
Mommo tilandiratu
Zopumitsa mtimawu.

Yesu munadzukanso
M’manda lero lomwetu;
Ntchito munayambayo
Yakudzutsa anthu ’fe,
Kuti ndi mitimayi
Tigwirebe ntchitozi.

Post navigation

Previous: Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
Next: Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 1209 Mnyamata wake ndinetu,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 165 ATATE,’nu, atate ’nu,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version