Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

 

MUNDIMVERE, Mbuye wanga
Nkana ine ndimalakwa,
Koma ndinu moyo wanga;
Mbuye, mkhale ndine.

Ndine mlendo pansi pano,
Msanditaye m’dzanja lanu,
Mundisunge mwana wanu;
Mbuye, mkhale ndine.

Munafera ine kale
Kuti mukandimasule,
Lero lino mndinyamule;
Mbuye, mkhale ndine.

Mundidzaze ndi chikondi,
Mndiyeretse m’mtima monse,
Chifuniro changa mthyole;
Mbuye, mkhale ndine.

Imfa ikandifikira,
Inu ndidzakangamira
Ndikaloŵa ine m’mdima,
Mbuye, mkhale ndine.

Post navigation

Previous: Hymn 390 A! YESU, ndapangana
Next: Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1850 Anthu a mitundu yonse,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version