Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

 

AITANA, aitana dziko lonse,
Imvani mukhaliranji chete?
Aitana,
Aitana aitana dziko lonse.

Mfumu iyi, Mfumu iyi ya Kumwamba
Ndi Yesu, ndi Mpulumutsiyo wa anthu onse.
Anthu onse, anthu onse, tinke kwawo.

Aitana,aitana inu mayi,
Ndi Yesu, amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu mayi.

Aitana, aitana inu ’tate,
Ndi Yesu amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu ’tate.

Yesu ati, Yesu ati; “Muzisiye
Zoipa zimene muzichita, muzisiye,
Muzisiye, muzisiye inu nonse.”

Titi bwanji? Titi bwanji ife anthu?
Ndi Yesu anatifera ife akuchimwa;
Akuchimwa, akuchimwa tinke kwawo.

Post navigation

Previous: Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
Next: Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 168 Yendani mwaulemerero,
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version