Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

 

AITANA, aitana dziko lonse,
Imvani mukhaliranji chete?
Aitana,
Aitana aitana dziko lonse.

Mfumu iyi, Mfumu iyi ya Kumwamba
Ndi Yesu, ndi Mpulumutsiyo wa anthu onse.
Anthu onse, anthu onse, tinke kwawo.

Aitana,aitana inu mayi,
Ndi Yesu, amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu mayi.

Aitana, aitana inu ’tate,
Ndi Yesu amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu ’tate.

Yesu ati, Yesu ati; “Muzisiye
Zoipa zimene muzichita, muzisiye,
Muzisiye, muzisiye inu nonse.”

Titi bwanji? Titi bwanji ife anthu?
Ndi Yesu anatifera ife akuchimwa;
Akuchimwa, akuchimwa tinke kwawo.

Post navigation

Previous: Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
Next: Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version