Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

  1. Home   »  
  2. Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

 

ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
Ŵalira Yesu m’ntchito zakozi,
Ŵalira Yesu pofanana ndi
Ambuyathu Yesu Kristu.

Tiŵaliretu, tiŵaliretu
Ambuye Yesu wotikonda ’fe;
Mlemekeze ’Ye tsiku lonseli,
Ine tiŵalire Yesu.

Ŵalira Yesu pazobvutazo,
Ŵalira Yesu pakukondwanso,
Ŵalira Yesu, imbirani ’nu
Ambuyathu Yesu Kristu.

Ŵalira Yesu wolimbitsayo,
Ŵalira Yesu m’moyo monsemo
Ŵalira Yesu; tidzaonatu
Ambuyathu Yesu Kristu.

Post navigation

Previous: Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
Next: Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 690 Mu ulemerero,
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version