Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

  1. Home   »  
  2. Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

 

ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
Ŵalira Yesu m’ntchito zakozi,
Ŵalira Yesu pofanana ndi
Ambuyathu Yesu Kristu.

Tiŵaliretu, tiŵaliretu
Ambuye Yesu wotikonda ’fe;
Mlemekeze ’Ye tsiku lonseli,
Ine tiŵalire Yesu.

Ŵalira Yesu pazobvutazo,
Ŵalira Yesu pakukondwanso,
Ŵalira Yesu, imbirani ’nu
Ambuyathu Yesu Kristu.

Ŵalira Yesu wolimbitsayo,
Ŵalira Yesu m’moyo monsemo
Ŵalira Yesu; tidzaonatu
Ambuyathu Yesu Kristu.

Post navigation

Previous: Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
Next: Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 423 Koma azibvala
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version