Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

  1. Home   »  
  2. Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

 

ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
Ŵalira Yesu m’ntchito zakozi,
Ŵalira Yesu pofanana ndi
Ambuyathu Yesu Kristu.

Tiŵaliretu, tiŵaliretu
Ambuye Yesu wotikonda ’fe;
Mlemekeze ’Ye tsiku lonseli,
Ine tiŵalire Yesu.

Ŵalira Yesu pazobvutazo,
Ŵalira Yesu pakukondwanso,
Ŵalira Yesu, imbirani ’nu
Ambuyathu Yesu Kristu.

Ŵalira Yesu wolimbitsayo,
Ŵalira Yesu m’moyo monsemo
Ŵalira Yesu; tidzaonatu
Ambuyathu Yesu Kristu.

Post navigation

Previous: Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
Next: Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1291 Njobvuta njira ndimayendamo,
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version