Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

 

PENYETSETSA Yesu,
Mtima wosauka; Anafera iwe,
Idza, nupumule.
Iye anachotsa
Nsoni ndi zoipa;
Penyetsetsa Yesu,
Ndi kukhulupira.

Penyetsetsa Yesu
Likatentha dzuŵa;
Yachuluka ntchito,
Mphamvu idzakula.
Akonzera kwawo
Nyumba zokhalamo;
Penyetsetsa Yesu,
Mtsatetu tsopano.

Penyetsetsa Yesu
Pogwirana nawo;
Nkhondo ikabvuta
Tamva Mbuye wako.
Achuluka’dani,
Iwe ungofoka;
Penyetsetsa Yesu,
Mantha adzachoka.

Ndipo pakuloŵa
M’dziko la Kumwamba,
Udzapeza komwe
Onse adzatama.
Mwa zoŵala zija
Za Kumwamba kwawo,
Udzapenya maso
Yesu Mbuye wako.

Post navigation

Previous: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
Next: Hymn 163 MALO anachepa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version