Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

 

PENYETSETSA Yesu,
Mtima wosauka; Anafera iwe,
Idza, nupumule.
Iye anachotsa
Nsoni ndi zoipa;
Penyetsetsa Yesu,
Ndi kukhulupira.

Penyetsetsa Yesu
Likatentha dzuŵa;
Yachuluka ntchito,
Mphamvu idzakula.
Akonzera kwawo
Nyumba zokhalamo;
Penyetsetsa Yesu,
Mtsatetu tsopano.

Penyetsetsa Yesu
Pogwirana nawo;
Nkhondo ikabvuta
Tamva Mbuye wako.
Achuluka’dani,
Iwe ungofoka;
Penyetsetsa Yesu,
Mantha adzachoka.

Ndipo pakuloŵa
M’dziko la Kumwamba,
Udzapeza komwe
Onse adzatama.
Mwa zoŵala zija
Za Kumwamba kwawo,
Udzapenya maso
Yesu Mbuye wako.

Post navigation

Previous: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
Next: Hymn 163 MALO anachepa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1330 Etu, zilira konseko
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version