Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

  1. Home   »  
  2. Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

 

Yesu, dzina lakukonda,
Lopambana onse ena,
Tonse tidzaligwadira
Ndi mitima yochepetsa.

Yesu, dzina lokondwetsa
Akuipa a padziko,
Kale linatidziŵitsa
Mpulumutsi ndiye Yesu.

Yesu dzina lakufatsa,
Anamutcha ’kali Mwana,
M’mene analoŵa kale
M’dziko lino lakudana.

Yesu, dzina ndi lomweli
La pa dziko lino lonse,
Ndi lamphamvu yolanditsa
Anthu mu masoka onse.

Yesu, dzina lakukonda
La Mwanayo wa Mulungu,
Ife anthu osauka
Tithaŵira nalo kwanu.

Post navigation

Previous: Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
Next: Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version