Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 308 AULENDO, munka kuti

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

 

AULENDO, munka kuti
Ndi zindodo m’manja mwanu?
Paulendo tizipita;
Aitana Mbuye wathu;
Pamapiri, pamadambo
Tizipita komwe kwawo.
Tizipita komwe kwawo
Kuli dzikolo labwino,
Tizipita komwe kwawo
Kuli dzikolo labwino.

Kodi simuopa njira,
Inu anthu akufoka?
Ayi, atiperekeza
Mbuye wathu wotikonda.
Iye amakhala nafe,
Natitsogolera ife.
Atitsogolera ife
Kuli dzikolo labwino.
Atitsogolera ife
Kuli dzikolo labwino.

Mundiuze, aulendo,
Muli chiani m’Mwamba muja?
Atibvekako zoyera
Akorona natininkha;
Moyo, moyo atipatsa,
Kwa Mulungu tidzakhala.
Kwa Mulungu tidzakhala
Kuli dzikolo labwino,
Kwa Mulungu tidzakhala
Kuli dzikolo labwino.

Kodi inu, aulendo,
Ife titsagane nanu?
Inde, mudze inu nonse,
Mudze nafe paulendo.
Inde, mutiperekeze,
Yesu atilinda ife.
Yesu atilinda ife
Kuli dzikolo labwino,
Yesu atilinda ife
Kuli dzikolo labwino.

Post navigation

Previous: Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
Next: Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version