Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 308 AULENDO, munka kuti

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 308 AULENDO, munka kuti

 

AULENDO, munka kuti
Ndi zindodo m’manja mwanu?
Paulendo tizipita;
Aitana Mbuye wathu;
Pamapiri, pamadambo
Tizipita komwe kwawo.
Tizipita komwe kwawo
Kuli dzikolo labwino,
Tizipita komwe kwawo
Kuli dzikolo labwino.

Kodi simuopa njira,
Inu anthu akufoka?
Ayi, atiperekeza
Mbuye wathu wotikonda.
Iye amakhala nafe,
Natitsogolera ife.
Atitsogolera ife
Kuli dzikolo labwino.
Atitsogolera ife
Kuli dzikolo labwino.

Mundiuze, aulendo,
Muli chiani m’Mwamba muja?
Atibvekako zoyera
Akorona natininkha;
Moyo, moyo atipatsa,
Kwa Mulungu tidzakhala.
Kwa Mulungu tidzakhala
Kuli dzikolo labwino,
Kwa Mulungu tidzakhala
Kuli dzikolo labwino.

Kodi inu, aulendo,
Ife titsagane nanu?
Inde, mudze inu nonse,
Mudze nafe paulendo.
Inde, mutiperekeze,
Yesu atilinda ife.
Yesu atilinda ife
Kuli dzikolo labwino,
Yesu atilinda ife
Kuli dzikolo labwino.

Post navigation

Previous: Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
Next: Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 1789 Nditani ine kubwezera Mbuye
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version