Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

  1. Home   »  
  2. Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

 

ANA akumwamba ndife,
Paulendo timaimba;
Timatama Mbuye wathu
Wa ulemerero wonse.

Tilikupita kwathu kuja
Munjira ya atate athu,
Amakondwera lero lomwe;
Tinka kuonana nawo.

Mbuye anatiitana
Kukagwira ntchito yake,
Kuitana anthu onse
Atsatenso njira yino.

Inde Mbuye, tibweradi,
Zathu zonse tizisiya,
Mtsogoleri wathu ndinu
Titsatabe inu nokha.

Post navigation

Previous: Hymn 308 AULENDO, munka kuti
Next: Hymn 310 MBUYE munditsogolere,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version