Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

  1. Home   »  
  2. Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

 

ANA akumwamba ndife,
Paulendo timaimba;
Timatama Mbuye wathu
Wa ulemerero wonse.

Tilikupita kwathu kuja
Munjira ya atate athu,
Amakondwera lero lomwe;
Tinka kuonana nawo.

Mbuye anatiitana
Kukagwira ntchito yake,
Kuitana anthu onse
Atsatenso njira yino.

Inde Mbuye, tibweradi,
Zathu zonse tizisiya,
Mtsogoleri wathu ndinu
Titsatabe inu nokha.

Post navigation

Previous: Hymn 308 AULENDO, munka kuti
Next: Hymn 310 MBUYE munditsogolere,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1310 Yesu wondikondadi,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 107 Panalibe mwa abale
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version