Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

  1. Home   »  
  2. Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

 

MKATI mwa zovuta zathu
Yesu aitana ife,
Tsiku lonse amanena:
“Tsata Ine mkristu iwe.”

Kale ophunzira ake
Namvanso kunyanja kwawo,
Zinthu zonse anasiya
Kukatsata Mbuye wawo.

Yesu atiuze ife;
Tikakonda chuma chokha,
Ati Yesu; “Mwana wanga,
Undikondetu koposa.”

Mwachimwemwe, mwachisoni,
Pogwiritsa ntchito zonse,
Aitana Mpulumutsi
Kuti tizimkonda tonse.

Yesu ayitana ife;
Mbuye, mutimvetse ndithu,
Tipereke mtima wathu,
Tikondane lero ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version