Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

  1. Home   »  
  2. Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

 

MKATI mwa zovuta zathu
Yesu aitana ife,
Tsiku lonse amanena:
“Tsata Ine mkristu iwe.”

Kale ophunzira ake
Namvanso kunyanja kwawo,
Zinthu zonse anasiya
Kukatsata Mbuye wawo.

Yesu atiuze ife;
Tikakonda chuma chokha,
Ati Yesu; “Mwana wanga,
Undikondetu koposa.”

Mwachimwemwe, mwachisoni,
Pogwiritsa ntchito zonse,
Aitana Mpulumutsi
Kuti tizimkonda tonse.

Yesu ayitana ife;
Mbuye, mutimvetse ndithu,
Tipereke mtima wathu,
Tikondane lero ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 488 M’MANJA a Yesu wanga
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version