Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

 

KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Ndi Iye Mlungu Wamphamvu;
Angelo anapembedza
Mwana wakhanda Iyeyu.

Kamwana kaja ’nayamba
Kuonetsera Atate,
Lero anena Kumwamba:
“Tiana tidze kwa Ine.”

Tibwera ndi tianato
Kukabatiza ’menewa;
Muŵachitire chifundo.
M’ŵapatse Mzimu Woyera.

Angelo anu asunga
Tiana tathu tofoka;
Pa njira yanu tiyenda,
Mulembe m’Mwamba maina.

Mukonda nyimbo za ana,
Kokoma amaimbatu;
Ndi ana athu atama
Atate, Mwana ndi Mzimu.

Post navigation

Previous: Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 351 Titi bwanji?
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version