Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

 

KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Ndi Iye Mlungu Wamphamvu;
Angelo anapembedza
Mwana wakhanda Iyeyu.

Kamwana kaja ’nayamba
Kuonetsera Atate,
Lero anena Kumwamba:
“Tiana tidze kwa Ine.”

Tibwera ndi tianato
Kukabatiza ’menewa;
Muŵachitire chifundo.
M’ŵapatse Mzimu Woyera.

Angelo anu asunga
Tiana tathu tofoka;
Pa njira yanu tiyenda,
Mulembe m’Mwamba maina.

Mukonda nyimbo za ana,
Kokoma amaimbatu;
Ndi ana athu atama
Atate, Mwana ndi Mzimu.

Post navigation

Previous: Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version