Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

 

USANABADWE, Yeremiya,
Ine ndinakudziwa;
Ndipo ndinakupatula,
Kuti ukhale mneneri.

Ulalike mawu anga Yeremiya,
Pita ukalalikire
Mawu anga;
Mawu anga Yeremiya.

“Usaopetu nkhope zawo,
Ine ndili ndi iwe;
Kuti ndikulanditsetu,
Iweyo,” ati Yehova.

Usaganize ndiwe mwana,
Iwe udzanka konse;
Kumene ndidzakutuma,
Kuti ukalalikire.

Post navigation

Previous: Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
Next: Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version