Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

 

KONDA dzinalo la Yesu,
Mwana wosawuka’we;
Ndilo lothandiza anthu,
Khala nalo ponse phee.

Dzina la Yesuyo,
N’lokondwetsa onsewo;
M’mwambamo, ponsepo,
Litonthoza m’mtimamo.

Konda dzinalo la Yesu,
M’moyo mwako monsemo;
Mmene ulikuyesedwa,
Tchula dzina lakelo.

Dzina ili ndi lokoma,
La Mtetezi wathuyo;
Mmene adzatilandira,
M’mwamba tidzakondwadi.

Mbuye Yesu tim’tamanda,
Ndi nyimbo zathu zonse;
Mfumu ya mafumu onse,
Yesu timayesadi.

Post navigation

Previous: Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
Next: Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 301 Mwanawankhosa
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 168 Yendani mwaulemerero,
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 692 Paulendo wathu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version