Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

 

KONDA dzinalo la Yesu,
Mwana wosawuka’we;
Ndilo lothandiza anthu,
Khala nalo ponse phee.

Dzina la Yesuyo,
N’lokondwetsa onsewo;
M’mwambamo, ponsepo,
Litonthoza m’mtimamo.

Konda dzinalo la Yesu,
M’moyo mwako monsemo;
Mmene ulikuyesedwa,
Tchula dzina lakelo.

Dzina ili ndi lokoma,
La Mtetezi wathuyo;
Mmene adzatilandira,
M’mwamba tidzakondwadi.

Mbuye Yesu tim’tamanda,
Ndi nyimbo zathu zonse;
Mfumu ya mafumu onse,
Yesu timayesadi.

Post navigation

Previous: Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
Next: Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 380 ATATE, muwapenya
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 580 Mwana wakuyera ‘Nu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version