Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

 

MKAZI wa ku Samariya,
Napita kukatunga madzi;
Pofika iyetu komweko,
Anapeza Ambuye Yesu.

Ambuye ananena:
“Ndipatseni madzi Ndimweko;
Ukanadziwa mtulo wa Mulunguyo,
Sukanandimana madzi.”

Ambuye nanena naye:
“Kayitane mwamuna wako;”
Mkazi anamuyankha nati:
“Inetu ndilibe mwamuna.”

Mkazi pochoka pomwepo,
Natsimikizatu mumtima;
Nati: “Uyu ndiye Mesiya,
Ndi Mwana wa Mulunguyotu.”

Abale tikhulupi’re,
Kuti Ambuye Yesuyo;
Ndiye Mwanadi wa Mulungu,
Ndiponso ndi Mpulumutsiyo.

Post navigation

Previous: Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
Next: Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version