Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

 

MKAZI wa ku Samariya,
Napita kukatunga madzi;
Pofika iyetu komweko,
Anapeza Ambuye Yesu.

Ambuye ananena:
“Ndipatseni madzi Ndimweko;
Ukanadziwa mtulo wa Mulunguyo,
Sukanandimana madzi.”

Ambuye nanena naye:
“Kayitane mwamuna wako;”
Mkazi anamuyankha nati:
“Inetu ndilibe mwamuna.”

Mkazi pochoka pomwepo,
Natsimikizatu mumtima;
Nati: “Uyu ndiye Mesiya,
Ndi Mwana wa Mulunguyotu.”

Abale tikhulupi’re,
Kuti Ambuye Yesuyo;
Ndiye Mwanadi wa Mulungu,
Ndiponso ndi Mpulumutsiyo.

Post navigation

Previous: Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
Next: Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version