Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 113 KALERO anthu onse

  1. Home   »  
  2. Hymn 113 KALERO anthu onse

Hymn 113 KALERO anthu onse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 113 KALERO anthu onse

 

KALERO anthu onse
Nachimwa kwa Mulungu
Mulungu anawona
Nawona tchimo lawo,
Nafuna kwawononga,
Nafuna kwawononga.

Mulungu anatuma,
Natuma mvula ija,
Nadzaza dziko lonse
Anafa anthu onse,
Anafa m’mvula muja,
Anafa m’mvula muja.

Mulungu anatuma,
Natuma Nowa uja,
Wamanga chombo chake,
Ndi chachitalitali,
Nowayo nayendamo,
Nowayo nayendamo.

Nowayo anatuma,
Natuma chikwangwala,
Chatsika pansi pansi,
Chosabwerera konse,
Chithaŵa m’talitali,
Chithaŵa m’talitali.

Kutuma wabwereza,
Natuma nkhunda ija,
Yatsika pamadzipo,
Yathyolatu mayani,
Yampatsa Nowa yemwe,
Yampatsa Nowa yemwe.

Kalelo Mbuye Yesu
’Nafera anthu onse,
Ndiyeyo chombo chathu,
Tikabisala mommo
Tipulumuka mommo,
Tipulumuka mommo.

Post navigation

Previous: Hymn 112 ELISA mneneri,
Next: Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 423 Koma azibvala

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version