Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

 

MUNASIYATU dziko lanulo,
E, chifukwa cha íne;
Ndi ku Betlehemuko,
Pakubadwa Inu,
M’nyumba zawo nakukanani.

Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga;
Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga.

Akumwambako nayimbitsatu,
Kukulemekezaní;
Koma monga mwana,
M’dziko munabadwa,
Munadzíchepetsadi.

Nyama za mthengo ndi mbalamezo,
Zili namo mogonamo;
Koma Mwana Mlungu,
Analibe nyumba,
M’mapululu nagonatu.

Munadzera ndi mawu amoyo,
Akupulumutsa anthu;
Anakaníza,
Anasautsa,
Anapachika Inu.

Mmene mubwera kutiŵeruza,
Ndi angelo oyimbira;
Mundiitane,
Muti, “Idza ‘we,
Khala nane Kumwamba.”

Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso;
Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso.

Post navigation

Previous: Hymn 38 ANGELO ayimba,
Next: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1184 Akondwerera nthawiyi
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version