Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,

 

MUNASIYATU dziko lanulo,
E, chifukwa cha íne;
Ndi ku Betlehemuko,
Pakubadwa Inu,
M’nyumba zawo nakukanani.

Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga;
Mbuye Yesu, lowani ‘mtima,
Nyumba yanu ndi mtima’nga.

Akumwambako nayimbitsatu,
Kukulemekezaní;
Koma monga mwana,
M’dziko munabadwa,
Munadzíchepetsadi.

Nyama za mthengo ndi mbalamezo,
Zili namo mogonamo;
Koma Mwana Mlungu,
Analibe nyumba,
M’mapululu nagonatu.

Munadzera ndi mawu amoyo,
Akupulumutsa anthu;
Anakaníza,
Anasautsa,
Anapachika Inu.

Mmene mubwera kutiŵeruza,
Ndi angelo oyimbira;
Mundiitane,
Muti, “Idza ‘we,
Khala nane Kumwamba.”

Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso;
Mtima wanga udzakondwera,
Mmene mundilandiranso.

Post navigation

Previous: Hymn 38 ANGELO ayimba,
Next: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 1312 Wina sindifuna ‘yi,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version