Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

  1. Home   »  
  2. Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,

 

’TATE wa Kumwambako,
Likayere Dzinalo,
Udzetu Ufumu wanu;
Chifuniro chanucho
Chichitike pansipa
Monga chachitika kwanu.

Mutipatse leroli
E, chakudya chathuchi
Tsiku n’tsiku tichilira.
Mukhululukiredi
Tchimo lathu, monga ’fe
Iwo adatichimwira.

Musatifikitsemo
Muli mayeserowo,
Koma mutipulumutse.
Wanu ndi ufumuwo,
Mphamvu ndi ulemunso
Kufikira nthaŵi zonse.

Post navigation

Previous: Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
Next: Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 1312 Wina sindifuna ‘yi,
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 351 Titi bwanji?
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version