Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

 

KUNALI munthu ku Yeriko,
Dzina lake Zakeyu;
Anali munthu wamkulu,
Wokhometsa misonkho.

(M) Kunali Zakeyu,
(O) Ku Yeriko,
(M) Nafunafuna,
(O) Kuwona Yesu,
(M) Koma chifukwa,
(O) Cha khamulo,
Anakwera mumtengo.

Paulendowo Ambuyeyo,
Anafika pamtengo;
Nayang’ana m’mwamba muja,
Anawona Zakeyu,

Ambuye Yesu nanenadi,
“Fulumira nutsike;
Lero lino ndiyenera,
Kukhala m’nyumba mwako.”

Zakoyuyo mofulumira,
Anatsika mumtengo,
Anam’tenga Mbuye Yesu,
Kuti akam’chereze,

Anadandauladi ena,
“Ambuye wachitanji?
Bwanji Iye analowa,
M’nyumba ya wochimwayo?”

Zakeyuyo pakumva ichi,
Anawuza Ambuye:
“Theka la chuma changacho,
Ndidzapatsa osowa.”

Leronso chipulumutsochi,
Chagwera m’nyumba yathu;
Tilape zoipa zathu,
Kutí tipulumuke.

Post navigation

Previous: Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
Next: Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 647 Tiyamike Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version