Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

 

KUNALI munthu ku Yeriko,
Dzina lake Zakeyu;
Anali munthu wamkulu,
Wokhometsa misonkho.

(M) Kunali Zakeyu,
(O) Ku Yeriko,
(M) Nafunafuna,
(O) Kuwona Yesu,
(M) Koma chifukwa,
(O) Cha khamulo,
Anakwera mumtengo.

Paulendowo Ambuyeyo,
Anafika pamtengo;
Nayang’ana m’mwamba muja,
Anawona Zakeyu,

Ambuye Yesu nanenadi,
“Fulumira nutsike;
Lero lino ndiyenera,
Kukhala m’nyumba mwako.”

Zakoyuyo mofulumira,
Anatsika mumtengo,
Anam’tenga Mbuye Yesu,
Kuti akam’chereze,

Anadandauladi ena,
“Ambuye wachitanji?
Bwanji Iye analowa,
M’nyumba ya wochimwayo?”

Zakeyuyo pakumva ichi,
Anawuza Ambuye:
“Theka la chuma changacho,
Ndidzapatsa osowa.”

Leronso chipulumutsochi,
Chagwera m’nyumba yathu;
Tilape zoipa zathu,
Kutí tipulumuke.

Post navigation

Previous: Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
Next: Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hello world!
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version