Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

 

KUNALI munthu ku Yeriko,
Dzina lake Zakeyu;
Anali munthu wamkulu,
Wokhometsa misonkho.

(M) Kunali Zakeyu,
(O) Ku Yeriko,
(M) Nafunafuna,
(O) Kuwona Yesu,
(M) Koma chifukwa,
(O) Cha khamulo,
Anakwera mumtengo.

Paulendowo Ambuyeyo,
Anafika pamtengo;
Nayang’ana m’mwamba muja,
Anawona Zakeyu,

Ambuye Yesu nanenadi,
“Fulumira nutsike;
Lero lino ndiyenera,
Kukhala m’nyumba mwako.”

Zakoyuyo mofulumira,
Anatsika mumtengo,
Anam’tenga Mbuye Yesu,
Kuti akam’chereze,

Anadandauladi ena,
“Ambuye wachitanji?
Bwanji Iye analowa,
M’nyumba ya wochimwayo?”

Zakeyuyo pakumva ichi,
Anawuza Ambuye:
“Theka la chuma changacho,
Ndidzapatsa osowa.”

Leronso chipulumutsochi,
Chagwera m’nyumba yathu;
Tilape zoipa zathu,
Kutí tipulumuke.

Post navigation

Previous: Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
Next: Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version