Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

  1. Home   »  
  2. Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

 

NDIDZE pafupi pa
Mlungu wanga,
Ngakhale pamtanda
Mundikweza;
Koma ndiimbabe
Mbuye mndikhalitse,
Mbuye mndikhalitse,
M’fupi Ndinu.

Ngakhale kuthengo
Ndasokera,
M’mdima ndigonapa
E, pamwala;
Koma m’kulotako
Ndiyandikizanso,
Ndiyandikizanso
M’fupi Ndinu.

Pajapo ndipenya
Pokwerapo,
Angelo atsika
Kumwambako,
Ndiwo akodola
Kuti ndikabwere,
Kuti ndikabwere
M’fupi Ndinu.

Tsopano poukanso
Wokondwatu,
Ndipeza pomwepo
Pali Mlungu;
Ndipo masautso
Andisendezanso,
Andisendezanso,
M’fupi Ndinu.

Pena pakufadi,
N’kwera m’Mwamba,
Dzuŵa ndi nyenyezi
Zitsalira;
Pomwe ndiimbanso,
Ndidza pafupi pa,
Ndidza pafupi pa
Mlungu wanga.

Post navigation

Previous: Hymn 301 MBUYE, ndapangana
Next: Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version