Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

 

TATE ndili mwana wanu,
Nkana ndinachimwa,
Ndingolirira kwa Inu;
Khululukireni.

Machimo anga ngambiri
Osaŵerengeka,
Ndingoyang’ana kwa Inu;
Khululukireni.

Ndinachimwa poganiza
Ndi polankhulanso,
M’ntchito zanga ndachimwanso;
Khululukireni.

Ndinachita mphulupulu,
Ndinakunyozani,
M’ntchito zanga ndalephera;
Khululukireni.

Zonse ndinakonda kale
Ndi zopanda pake,
Sindinakhuta nazotu;
Khululukireni.

Post navigation

Previous: Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
Next: Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 563 Ndipo Mwana uyu Yesu
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 444 Mpemphe Mbuye asunge
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version