Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

 

DZIKO lino lapansi,
Moyo ndi wovuta;
Nthawi zina kuseka,
Nthawi zina kulira;
Komatu Ambuye wathu,
Amatisamalira;
Mbale wanga pilira.

Pilira, pilira, mbale wanga pilira,
Dziko lino ndi lovuta
Mbale wanga pilira;
Linadana naye Mwana wa Mulungu,
Mbale wanga pilira.

Zabwino zimabwera,
Ndipo zimapita;
Dziwa kuti Ambuye,
Afunitsa iwedi;
Kuti ugwiretu ntchito,
Yakeyi m’dziko lino;
Mbale wanga pilira.

Tsikulo lilinkudza,
Lomwe Mbuye Yesu;
Adzanena kwa iwe,
Bwera upumuletu;
Kuzovuta ndi zowawa,
Zam’dziko lapansili;
Mbale wanga pilira.

Post navigation

Previous: Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
Next: Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version