Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

  1. Home   »  
  2. Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

 

ATATE, tifika pamaso panu;
Mukomane ndi ife, Mbuye wathu.

Mitima yathu iyi nayo njanu,
Muiyeretse, muikonze Mbuye.

Ndi maso athu awa nawo nganu,
Muŵapenyetse zinthu zanu zokha.

Ndi manja athu awa nawo nganu,
Agwiretu ntchito yanu yokhayo.

Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
Ithamange m’ntchito yanu yokhayo.

Ndi milomo yathu iyinso njanu,
Ilalike Mawu anu kwa onse.

Ndi makutu athu awanso nganu,
Muŵamvetse Mawu anu okhawo.

Tidziperekadi konse kwa Inu
Tikakhale anthu anu okhawo.

Post navigation

Previous: Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
Next: Hymn 355 DZIKO lonse mlambire

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version