Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

 

NDI lokoma m’Mwambamo,
Mbuye, Bwalo lanulo;
Ndi mwabwino muli ’Nu
Dziko losachimwali;
Mtima wana wonsewu
Umakhumba m’Mwambamo
Nkhope ya Mbuyathuyu,
Mlungu wa chisomoyo.

Zimbalame zonsezi
Zimayamikira ’Nu;
Anthu amakondwanso
Okhumbira m’Mwambamo;
Njiŵa yosapumayo
Inafika m’chombocho;
Okhulupirira ’Nu
Amapuma kwanuno.

Anthu opembedzawo
Amakondwa m’mtimamo;
Munapatsa madzitu,
Munagwetsa manawo;
Mumakoma mtimatu
Tidzayamikiratu,
Pachimpando chanucho
Mkhale Mfumu yathudi.

Post navigation

Previous: Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
Next: Hymn 375 YESU m’khale nafe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 351 Titi bwanji?
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 1291 Njobvuta njira ndimayendamo,
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version