Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,

Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,

 

MLENGI wathu Woyeranu,
Mutimvere ‘fe;
M’wasungire akutali,
Bwinodi.

Mbuye Yesu,
m’yandikire,
M’wakondwetsebe;
Mulimbitse mphamvu zawo,
Zonsezo.

Akawona masautso,
M’khale nawodi;
Akondwere mwachikondi,
Chanucho.

Mpulumutsi wakukoma,
Muwagwirize;
Nsiku zonse akulemekezeni,
(Akule-mekezeni.)

Mzimu wanu Woyerawo,
Awayeretse;
Agonjetse ndi chisomo,
M’nkhondoyi.

Tate, Mwana, Mzimu, ndi ‘Nu,
Mlungu mmodzitu;
Muwasunge mfupi mwanu,
Ponsepo.

Post navigation

Previous: Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
Next: Hymn 450 YESU, munditsogoza

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version