Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 450 YESU, munditsogoza

  1. Home   »  
  2. Hymn 450 YESU, munditsogoza

Hymn 450 YESU, munditsogoza

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 450 YESU, munditsogoza

 

YESU, munditsogoza
M’njira yanga yonseyo;
Wakunditsogozatu
Ndinu, mundisungetu;
Inde, paulendowo
Mundisunge kolimba.

Monga may’asusunza
Mwana wake polira,
Wakunditonthozatu
Ndinu, munditonthoze,
Ine, m’njira yanuyi
Munditsogoleretu.

Mbuye, ndinu wamphamvu,
Mumatola ananu.
Anthu onse pansipa
Ali otaikatu;
Muchitire chifundo,
Muŵatole onsewo.

Post navigation

Previous: Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
Next: Hymn 451 MLUNGU alinane;

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version