Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

 

MIPINGO iyo idzatu,
Yoyenda mangu pajapo,
Afuma kuti anthuwo?
Afika bwanji komweko?

Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo.”
Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo”

Azizwa anthu ajawo,
Nafunsa, “Ndani mlendoyo?
Wanzeru monga Iyeyo
Kulibe wina konseko.”

Ndi Yesu yemwe kalelo,
’Nakhala munthu pansipa;
Anthenda onsenthaŵiyo
Nachirayake mphamvuyo

Afika Yesu leroli,
Chifundo m’mtima wakemo,
Timfitse msanga kwathuko
Akhale nafe ponsepo.

Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
Timyese Mfumu yathuyo,
Chifukwa tikamkanatu
Tikhala otayikawo.

Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo.
Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo

Post navigation

Previous: Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
Next: Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version