Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

  1. Home   »  
  2. Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

 

MBUYE ndamva mwawazira
Anthu ena madalitso;
Mvula yanu yawagwera;
Mbuye, ine mudalitse.

Etu ine, etu ine,
Mbuye, ine mudalitse.

’Tate, msandipitirire,
Ndimaipa mtima ine;
Ndiyenera munditaye,
Koma mukhululukire.

Yesu, msandipitirire
Kuti ndinu ndikondane;
Ndinalira Inu Mbuye,
Msandileke poitana.

Mzimu, msandipitirire,
Mupenyetsatu akhungu
Mboniyo ya Mbuye Yesu,
Mundipatse ine mphamvu.

Ndinagona mwa zoipa,
Ndinakunyozani ine,
Dziko lino ndinakonda,
Mbuye, mukhululukire.

Ha! chikondi cha Mulungu,
Mwazi wa Mbuyathu Yesu,
Chiyanjano cha Mzimuyo
Zonse zidzalemekeza.

Post navigation

Previous: Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
Next: Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version