Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

  1. Home   »  
  2. Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

 

MBUYE ndamva mwawazira
Anthu ena madalitso;
Mvula yanu yawagwera;
Mbuye, ine mudalitse.

Etu ine, etu ine,
Mbuye, ine mudalitse.

’Tate, msandipitirire,
Ndimaipa mtima ine;
Ndiyenera munditaye,
Koma mukhululukire.

Yesu, msandipitirire
Kuti ndinu ndikondane;
Ndinalira Inu Mbuye,
Msandileke poitana.

Mzimu, msandipitirire,
Mupenyetsatu akhungu
Mboniyo ya Mbuye Yesu,
Mundipatse ine mphamvu.

Ndinagona mwa zoipa,
Ndinakunyozani ine,
Dziko lino ndinakonda,
Mbuye, mukhululukire.

Ha! chikondi cha Mulungu,
Mwazi wa Mbuyathu Yesu,
Chiyanjano cha Mzimuyo
Zonse zidzalemekeza.

Post navigation

Previous: Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
Next: Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 423 Koma azibvala
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 447 Usachimwe konse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version