Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 9 TAMANI Ambuye,

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

 

TAMANI Ambuye,
Wamphamvu ndi Iye;
Akhala m’ulemu,
Kumwamba komweko.
Chikopa cholimba,
Ndi kothaŵiranso;
Kwa anthu akewo,
Kotero ndi Mlungu.

Uzani zamphamvu,
Imbani chisomo;
Za Mwini ulemu,
Ambuye wathuyo.
Poomba chimphepo
Mvulanso ndi bingu;
Padziko, pathambo,
Akhala ponsepo.

Zozizwa zam’dziko,
Za M’mwamba zonsezi;
Mulungu wamphamvu,
Munalenga zonse;
Muyendetsa mwezi,
Nyenyezi ndi dzuŵa;
Zolengedwa zonse,
Zimvera Ambuye.

Sitiha ifedi,
Kukamba zokoma;
Za Inu Mulungu,
Wolera anthuwa.
Zifika ndi mphepo,
Ndi mvula ndi dzuŵa;
Zigwera ponsepo,
Pa anthu onsewa.

Wamphamvu yosatha,
Chikondichangwiro;
Angelo akonda,
Kutama Mulungu.
Ndiponso ifetu,
Ana ‘nu tonse ‘fe;
Tiimba nyimboyi,
Yotama Ambuye.

Post navigation

Previous: Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
Next: Hymn 10 TSOPANO linoli,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1490 Musachitenso nthantha ‘yi,
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 85 MASO ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 380 ATATE, muwapenya
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version