Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

  1. Home   »  
  2. Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

 

MKRISTU, ulimbike
M’ntchito yakeyo;
Yesu anafera
Anthu akewo.

Mphamvu zathu zonse
Tionetsenso,
Kuti kudziŵike
Tili akewo.

Mtima wakufatsa
Amakondako;
Ndipo anthu onse
Angatengero.

Mapemphero athu
Tikakwezebe,
Dzina lake lomwe
Tiyamike ’fe.

Limbikani nonse
Mpaka imfayo.
Ndipo Mfumu yathu
Idzakondwatu.

Post navigation

Previous: Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
Next: Hymn 277 GWIRA zintchito zako,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 423 Koma azibvala
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version