Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

 

DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
Ndili ndekha mpanjira n’kwaŵenitu;
Ndilibetu chakudya, ndilibetu chakumwa,
Ndingoyenda mpanjira n’kwaŵenitu.

N’kwawenitu,
N’kwawenitu,
Dziko lino sikwathu
N’kwaŵenitu.

Dziko lino lapansi mavuto ndi osatha,
Ine sindingalithe n’kwaŵenitu;
Ukasowa chumacho, abwenzi akuthawa,
Koma kwathu satero n’kwaŵenitu.

Anyamata, ‘sungwana
Samaopa Mulungu,
Sichifukwa chinanso n’kwaŵenitu;
Abambo ndi amayi
Samaopa Mulungu,
Sichifukwa chinanso n’kwaŵenitu.

Tiyeni abale ‘fe tiyang’ane kwa Yesu,
Yemwe angatipatse moyowotu;
Moyo uno wam’dziko abale ndi wozunza,
Moyo wokoma ndiwo wa Yesuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
Next: Hymn 72 YESU wakukoma mtima,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hello world!
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 97 TIYAMIKE Mlunguyo,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version