Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,

 

LAMBIRA, Mfumuyo,
Ndi Yesu Mbuyathu,
Tamvani nyimbo za ‘mithenga aKumwambako;
Nafenso pansipa
Tim’yamikire ’Ye,
Ndi Mpulumutsi wathu wotifera kalero.

Lambira Yesuyo,
Wokonda tonsefe;
Mabala ake achikondi awonekabe;
Tisayiwale ’yi
Zoŵaŵa zakezo,
Tileke kum’chimwira, kum’sautsa Yesuyo.

Lambira Yesuyo,
Uthenga wakewu
Uyanjanitsa anthu onse m’dziko munomo:
Amaiŵala za
Kudana kwawoko,
Nayamikira Mfumu yamtendere monsemo.

Lambira Mfumuyo
Wolenga zonsezi:
Nyenyezi, dziko, dzuŵa, mwezi ndi mitamboyi;
Tikweze dzinalo
La Mbuye Yesuyo,
Tim’yamikire pansi pano ndi Kumwambako.

Post navigation

Previous: Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
Next: Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version