Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

 

AMITHENGA a Mulungu,
Anaimba nyimbo yomwe,
Posonkhana m’mlengalenga,
Natitu usiku womwe;
“Onse azilemekeza
Mlungu Wakumwambamwamba;
Akhalebe ndi mtendere
Anthu ali ponseponse.”

Amithenga anaimba
Ndi usiku m’mlengalenga.

Anamva abusa omwe
Anaŵeta nkhosa zawo.
Mthenga nati:
“Musaope;
Mumve ndikufotokoza:
Wabadwa usiku uno Yesu Kristu Ambuyathu
Ndiye Mpulumutsi wathu;
Anabadwa m’Betlehemu.”

Amithenga anaimba
Ndi usiku m’mlengalenga.

Yesu ndinu Mbuye wathu,
Munasiya za Kumwamba;
Munakhala mwana kuno;
Mnatifera mwaufulu.
Inu nonse amithenga,
Inu mumtamande Iye;
Anthu onse ali pansi Adza akondane naye.

Zoonazi amithenga
Anaimba m’mlengalenga.

Post navigation

Previous: Hymn 33 OWONADI mtima,
Next: Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version