Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

 

AMITHENGA a Mulungu,
Anaimba nyimbo yomwe,
Posonkhana m’mlengalenga,
Natitu usiku womwe;
“Onse azilemekeza
Mlungu Wakumwambamwamba;
Akhalebe ndi mtendere
Anthu ali ponseponse.”

Amithenga anaimba
Ndi usiku m’mlengalenga.

Anamva abusa omwe
Anaŵeta nkhosa zawo.
Mthenga nati:
“Musaope;
Mumve ndikufotokoza:
Wabadwa usiku uno Yesu Kristu Ambuyathu
Ndiye Mpulumutsi wathu;
Anabadwa m’Betlehemu.”

Amithenga anaimba
Ndi usiku m’mlengalenga.

Yesu ndinu Mbuye wathu,
Munasiya za Kumwamba;
Munakhala mwana kuno;
Mnatifera mwaufulu.
Inu nonse amithenga,
Inu mumtamande Iye;
Anthu onse ali pansi Adza akondane naye.

Zoonazi amithenga
Anaimba m’mlengalenga.

Post navigation

Previous: Hymn 33 OWONADI mtima,
Next: Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 1310 Yesu wondikondadi,
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version