Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 468 NDIKONDWA kuti

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

 

NDIKONDWA kuti
Atate wa M’mwamba,
Atidziwitsa chikondi chakecho;
Ndimaŵerenga m’Uthenga Wabwino,
Kuti Ambuye akonda ana ‘ke.

Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Yesu akonda, andikondabe;
Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Amandikondabe.

Yesu ndim’konda, akondanso ine,
Anandifera pamtanda woopsa;
Wosayenera, woipa ndi
Tsoka langalo Ambuye nachotsa.

Mzimu Woyera akhala mwa ine,
Atsimikiza chikondi cha Yesu:
Ine n’tachimwa amandikumbutsa,
“Lapa mwana we akukonda Yesu.”

Ndikadzawona Ambuye Kumwamba,
Sindidzawopa pokhala akonda:
Anandikonzera kalelo nyumba,
Ndidzakhalamo wokondwa, wokoma.

Post navigation

Previous: Hymn 467 NGOLIZO zilira
Next: Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 635 Tipempha madalitso ano mpatse ife tonse;
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version