Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 468 NDIKONDWA kuti

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

 

NDIKONDWA kuti
Atate wa M’mwamba,
Atidziwitsa chikondi chakecho;
Ndimaŵerenga m’Uthenga Wabwino,
Kuti Ambuye akonda ana ‘ke.

Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Yesu akonda, andikondabe;
Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Amandikondabe.

Yesu ndim’konda, akondanso ine,
Anandifera pamtanda woopsa;
Wosayenera, woipa ndi
Tsoka langalo Ambuye nachotsa.

Mzimu Woyera akhala mwa ine,
Atsimikiza chikondi cha Yesu:
Ine n’tachimwa amandikumbutsa,
“Lapa mwana we akukonda Yesu.”

Ndikadzawona Ambuye Kumwamba,
Sindidzawopa pokhala akonda:
Anandikonzera kalelo nyumba,
Ndidzakhalamo wokondwa, wokoma.

Post navigation

Previous: Hymn 467 NGOLIZO zilira
Next: Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 829 Titamadi ‘Tate,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version