Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 467 NGOLIZO zilira

  1. Home   »  
  2. Hymn 467 NGOLIZO zilira

Hymn 467 NGOLIZO zilira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 467 NGOLIZO zilira

 

NGOLIZO zilira
Za ’mithengawo,
Ndi zipata zonse
Zatsegudwa mbee!
Kristu, Mfumu yathu,
Mbuye wathudi,
Wapambana monse,
Alamulabe.

Ntchito zake zatha,
Timwimbiretu;
Yesuyo wakwera,
Timtamandetu.

’Natipulumutsa
Natiferako,
Ali mfumu ndithu
Kwa Atatewo;
Osasautsidwa,
Osafanso ’yi
Yesu, Mfumu yathu
Adakweradi.

Atipempherera
M’malo ’dalawo,
Tinke kwathu komwe
Ndi chisomocho;
Akonzera malo
Ana akewo;
Yesu alipobe,
Atikondanso.

Post navigation

Previous: Hymn 466 OSANATU, osana,
Next: Hymn 468 NDIKONDWA kuti

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version